letra de plan - praise umali
[verse 1: praise umali]
i worried all the time
i thought i’m running out of time
can’t take it a day at a time sometimes
man our dreams have been too loud since
we were only young kids
and now, we grown they loud still
i know ndizambiri umafuna mtima
nde pena mantha ankadzandigwila
like what if we don’t make it (yeah yeah)
what if we don’t make it (yeah yeah)
[chorus: praise umali]
koma tachoka nkutali
mulungu -n-li ndi pulani
pulani
inu zonse ndi nthawi
mulungu -n-li ndi pulani
pulani
yopanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
yopanga za ifeyo
akupanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
akupanga za ifeyo
[verse 2: gwamba]
yoh
venue yomweyo ena amaflopa
samatrenda nyimbo zawo akadropa
nde pena pride imafuna idzindikopa
koma mbuye w-nga sangakondwe kuti nzizipopa
nde rule number 1, k-makhala humble
poti ukazikweza amasiya kupanga zako
rule number 2, osakhala ndi tsankho
poti lero ndi kape mawa ali pamwamba pako
nkayang’ana k-mbuyo ngati ndingokuwa mbuye
ndinakhonza chani kuti inu mundimasule
mwandichotsa kutali kwinakunso mulambule
ulendowu ndiwautali koma
[chorus: praise umali]
koma tachoka nkutali
mulungu -n-li ndi pulani
pulani
inu zonse ndi nthawi
mulungu -n-li ndi pulani
pulani
yopanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
yopanga za ifeyo
akupanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
akupanga za ifeyo
letras aleatórias
- letra de 多想在平庸的生活擁抱你 - 隔壁老樊
- letra de wolf creek part ii (feat. schizo) - unaverage gang
- letra de any which way - senseless things
- letra de ja još uvek verujem - natasa bekvalac
- letra de антисоциальный (antisocial) - hapa (rus)
- letra de behind the flowers - joiner
- letra de he says - jonathan larson
- letra de rip this world - nicole saboune
- letra de toxic! - prince austin
- letra de mi placer (old version) - son de maik