
letra de aphiri - faith mussa
[verse 1]
a phiri anabwera kuchoka ku harare
a phiri anabwera kuchoka ku harare
pobwera k-meneko anabwera ndi suitcase
pobwera k-meneko anabwera ndi suitcase
koma mkati mwa suitcase munalibe kanthu shuwa
ndati mkati mwa suitcase munalibe kanthu shuwa
[pre-chorus]
a phiri anaganiza “kodi ndidzayenda kuti?”
makolo anga onse anamwalira ku dara
a phiri anaganiza “kodi ndidzayenda kuti?”
makolo anga onse anamwalira ku dara
koma mkati mwa suitcase munalibe kanthu shuwa
ndati mkati mwa suitcase munalibe kanthu shuwa
a phiri anaganiza “kodi ndizayenda kuti?”
makolo anga onse anamwalira ku dara
a phiri anaganiza “kodi ndizayenda kuti?”
makolo anga onse anamwalira ku dara
[chorus]
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
[pre-chorus]
a phiri anaganiza “kodi ndizayenda kuti?
a phiri anaganiza “kodi ndizayenda kuti?
ndati phiri anaganiza “kodi ndizayenda kuti?
koma mkati mwa suitcase munalibe kanthu shuwa
[chorus]
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
a phiri eh
letras aleatórias
- letra de home - brooke nicholls
- letra de ting a ling - gon cozy
- letra de lookin' back - valee & chasethemoney
- letra de the speakers - cornflames
- letra de education - pyrorca
- letra de milano - snipe
- letra de twisted - aaron taos
- letra de or pur - youri
- letra de lern zu chilln - marvin game
- letra de lue zersch wohär dass dr wind wääit - züri west